Deuteronomo 27:17-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Wotembereredwa iye wakusendeza malire a mnansi wace. Ndi anthu onse anene, Amen.

18. Wotembereredwa wakusokeretsa wakhungu m'njira, Ndi anthu onse anene, Amen.

19. Wotembereredwa iye wakuipsa mlandu wa mlendo, mwana wamasiye, ndi mkazi wamasiye. Ndi anthu onse anene, Amen.

Deuteronomo 27