Deuteronomo 26:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kuti akukulitseni koposa amitundu onse anawalenga, wolemekezeka, womveka dzina, ndi waulemu; ndi kuti mukhale mtundu wa anthu wopatulikira Yehova Mulungu wanu monga ananena.

Deuteronomo 26

Deuteronomo 26:11-19