Ahebri 9:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo cingakhale cipangano coyambaci cinali nazo zoikika za kulambira, ndi malo opatulika a pa dziko lapansi.

2. Pakuti cihema cidakonzeka, coyamba cija, m'menemo munali coikapo nyali, ndi gome, ndi mkate woonekera; paja paitanidwa Malo Opatulika,

3. Koma m'kati mwa cophimba caciwiri, cihema conenedwa Malo Opatulikitsa;

Ahebri 9