1 Mafumu 11:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

a mitundu ija Yehova adanena ndi ana a Israyeli za iwo, kuti, Inu musakalowa kwa iwo, ndipo iwo asadzalowe kwa inu; zedi adzatembenuza mitima yanu kutsata milungu yao; amenewo Solomo anawaumirira kuwakonda.

1 Mafumu 11

1 Mafumu 11:1-10