Yoweli 3:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndidzasonkhanitsa amitundu onse, ndi kutsikira nao ku cigwa ca Yosafati; ndipo ndidzaweruzana nao komweko za anthu anga, ndi colowa canga Israyeli, amene anawabalalitsa mwa amitundu, nagawa dziko langa,

Yoweli 3

Yoweli 3:1-7