Yohane 7:5-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Pakuti angakhale abale ace sanakhulupirira iye.

6. Cifukwa cace Yesu ananena nao, Nthawi yanga siinafike; koma nthawi yanu yakonzeka masiku onse.

7. Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilicitira umboni, kuti nchito zace ziri zoipa,

Yohane 7