Yohane 5:45-47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

45. Musayesa kuti Ine ndidzakunenezani inu kwa Atate; 6 pali wakukunenezani, ndiye Mose, amene inu mumtama.

46. Pakuti mukadakhulupirira Mose, mukadakhulupirira Ine; 7 pakuti iyeyu analembera za Ine.

47. Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?

Yohane 5