Yobu 5:17-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Taona, wodala munthu amene Mulungu amdzudzula;Cifukwa cace usapeputsa kulanga kwa Wamphamvuyonse.

18. Pakuti apweteka, namanganso mabala;Alasa, ndi manja ace omwe apoletsa.

19. Adzakupulumutsa m'masautso asanu ndi limodzi;Cinkana mwa asanu ndi awiri palibe coipa cidzakukhudza.

Yobu 5