Yobu 42:16-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ndipo zitatha izi, Yobu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi mphambu makumi anai, naona ana ace ndi zidzukulu zace mibadwo inai.

17. Namwalira Yobu, wokalamba ndi wa masiku ocuruka.

Yobu 42