Yobu 26:7-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Ayala kumpoto popanda kanthu, Nalenjeka dziko pacabe.

8. Amanga madzi m'mitambo yace yocindikira;Ndi mtambo sung'ambika pansi pace,

9. Acingira pa mpando wace wacifumu,Nayalapo mtambo wace.

10. Analembera madziwo malire,Mpaka polekeza kuunika ndi mdima.

11. Mizati ya thambo injenjemera,Ndi kudabwa pa kudzudzula kwace.

Yobu 26