Yobu 20:28-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Phindu la m'nyumba mwace lidzacoka,Akatundu ace adzamthawa tsiku la mkwiyo wace.

29. Ili ndi gawo la munthu woipa, locokera kwa Mulungu,Ndi colowa amuikiratu Mulungu.

Yobu 20