Yobu 19:11-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Wandiyatsiranso mkwiyo wace,Nandiyesera ngati wina wa adani ace.

12. Ankhondo ace andidzera pamodzi, nandiundira njira yao,Nandimangira misasa pozinga hema wanga.

13. Iye anandicotsera abale anga kutali,Ndi odziwana nane andiyesa mlendo konse.

14. Anansi anga andisowa,Ndi odziwana nane bwino andiiwala.

15. Iwo a m'nyumba mwanga ndi adzakazi anga andiyesa mlendo;Ndine wacilendo pamaso pao.

Yobu 19