Yobu 13:18-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Taonani tsono, ndalongosola mlandu wanga;Ndidziwa kuti adzandimasula ndiri wolungama,

19. Ndaniyo adzatsutsana nane?Ndikakhala cete, ndidzapereka mzimu wanga.

20. Zinthu ziwiri zokha musandicitire,Pamenepo sindidzabisalira nkhope yanu:

21. Mundicotsere dzanja lanu kutali,Ndi kuopsa kwanu kusandicititse mantha.

Yobu 13