Yesaya 7:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndipo Yehova ananenanso kwa Ahazi nati,

11. Udzipemphere wekha cizindikilo ca kwa Yehova Mulungu wako; pempha cam'mwakuya, kapena cam'mwamba.

12. Koma Ahazi anati, Sindipemphai ngakhale kumyesa Yehova.

13. Ndipo iye anati, Mverani inu tsopano, inu a nyumba ya Davide; kodi ndi kanthu kakang'ono kwa inu kutopetsa anthu, kuti inu mutopetsa Mulungu wanga?

Yesaya 7