Yeremiya 32:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli atero; Tenga akalata awa, kalata uyu wogulira, wosindikizidwa, ndi kalata uyu wobvundukuka, nuwaike m'mbiya yadothi; kuti akhale masiku ambiri.

Yeremiya 32

Yeremiya 32:13-20