Yeremiya 11:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, kuti,

2. Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu;

3. ndi kunena kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Aisrayeli: Wotembereredwa ndi munthu wosamvera mau a pangano ili,

Yeremiya 11