Oweruza 19:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo taonani, munthu nkhalamba anacokera ku nchito yace kumunda madzulo; munthuyu ndiye wa ku mapiri a Efraimu, nagonera ku Gibeya; kuma anthu pamenepo ndiwo Abenjamini.

Oweruza 19

Oweruza 19:10-17