Oweruza 19:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, masiku aja, pamene panalibe mfumu m'Israyeli, panali munthu Mlevi wogonera kutseri kwa mapiri a Efraimu amene anadzitengera mkazi wamng'ono wa ku Betelehemu-Yuda.

Oweruza 19

Oweruza 19:1-3