Oweruza 11:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali pakutha miyezi iwiri, anabwerera kwa atate wace amene anamcitira monga mwa cowinda cace anaciwinda; ndipo sanamdziwa mwamuna. Motero unali mwambo m'Israyeli,

Oweruza 11

Oweruza 11:35-40