Numeri 7:27-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwana wa nkhosa mmodzi wa caka cimodzi, zikhale nsembe yopsereza;

28. tonde mmodzi akhale nsembe yaucimo;

29. ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ana a nkhosa asanu a caka cimodzi; ndico copereka ca Eliyabu mwana wa Heloni.

30. Tsiku lacinai Elizuri, mwana wa Sedeuri, kalonga wa ana a Rubeni:

Numeri 7