Numeri 28:29-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. limodzi la magawo khumi likhale la mwana wa nkhosa mmodzi, momwemo ndi ana a nkhosa asanu ndi awiri;

30. tonde mmodzi wakutetezera inu.

31. Mupereke izi pamodzi ndi nsembe yopsereza yosalekeza, ndi nsembe yace yaufa, zikhale kwa inu zopanda cirema, ndi nsembe zace zothira.

Numeri 28