39. Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.
40. Ana a Imeri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
41. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
42. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
43. A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyeli, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.