Nehemiya 7:21-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Ana a Aberi, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi atatu.

22. Ana a Hasumu, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

23. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza anai.

24. Ana a Harifi, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

Nehemiya 7