Mlaliki 5:5-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Kusawinda kupambana kuwinda osacita,

6. Usalole m'kamwa mwako mucimwitse thupi lako; usanene pamaso pa mthenga kuti, Ndinaphophonya; Mulungu akwiyire mau ako cifukwa ninji, naononge nchito ya manja ako?

7. Pakuti monga mu unyinji wa maloto muli zacabe motero mocuruka mau; koma dziopa Mulungu.

Mlaliki 5