Miyambi 9:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Woweruza munthu wonyoza adzicititsa yekha manyazi;Yemwe adzudzula wocimwa angodetsa mbiri yace yace.

8. Usadzudzule wonyoza kuti angakude;Dzudzula wanzeru adzakukonda.

9. Ukacenjeza wanzeru adzakulitsa nzeru yace;Ukaphunzitsa wolungama adzaonjezera kuphunzira,

Miyambi 9