Miyambi 8:23-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Anandiimika cikhalire ciyambire,Dziko lisanalengedwe.

24. Pamene panalibe zozama ndinabadwa ine,Pamene panalibe akasupe odzala madzi.

25. Mapiri asanakhazikike,Zitunda zisanapangidwe, ndinabadwa;

26. Asanalenge dziko, ndi thengo,Ngakhale ciyambi ca pfumbi la dziko.

Miyambi 8