Miyambi 31:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Wofuna kufa umpatse cakumwa caukali,Ndi vinyo kwa owawa mtima;

7. Amwe, narwale umphawi wace, Osakumbukiranso bvuto lace.

8. Tsegula pakamwa pako, ukanenere wosalankhula,Ndi mlandu wa amasiye onse.

Miyambi 31