1. Yemwe aumitsa khosi atadzudzulidwa kwambiri,Adzasweka modzidzimuka, palibe comciritsa.
2. Pocuruka olungama anthu akondwa;Koma polamulira woipa anthu ausa moyo.
3. Mwamuna wokonda nzeru akondweretsa atate wace;Koma wotsagana ndi akazi adama amwaza cuma.
4. Mfumu akhazikitsa dziko ndi ciweruzo;Koma wosonkhetsa anthu mphatso alipululutsa.