Miyambi 26:21-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Monga makala ozizira pa makala akunyeka, ndi nkhuni pamoto;Momwemo munthu wamakangano autsa ndeu.

22. Mau a kazitape ndi zakudya zolongosokaZitsikira m'kati mwa mimba.

23. Milomo yofunitsitsa ndi mtima woipaIkunga mbale yadothi anaimata ndi mphala yasiliva.

Miyambi 26