18. Wocimwa ndiye ciombolo ca wolungama;Ndipo waciwembu adzalowa m'malo mwa oongoka mtima.
19. Kukhala m'cipululu kufunikaKuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wong'ung'udza.
20. Mokhala wanzeru muli katundu wofunika ndi mafuta;Koma wopusa angozimeza.
21. Wolondola cilungamo ndi cifundoApeza moyo, ndi cilungamo, ndi ulemu.