Miyambi 1:18-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Ndipo awa abisalira mwazi wao wao, alalira miyoyo yao yao.

19. Mayendedwe a yense wopindula cuma monyenga ngotere;Cilanda moyo wa eni ace,

20. Nzeru ipfuula panja;Imveketsa mau ace pabwalo;

21. Iitana posonkhana anthu polowera pacipata;M'mudzi inena mau ace;

Miyambi 1