Mateyu 3:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiponso tsopano lino nkhwangwa yaikidwa pa mizu ya mitengo; cifukwa cace mtengo uli wonse wosabala zipatso zabwino udulidwa nuponyedwa pamoto,

Mateyu 3

Mateyu 3:6-15