Mateyu 28:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Koma ophunzira khumi ndi mmodziwo anamuka ku Galileya, kuphiri kumene Yesu anawapangifa.

17. Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.

18. Ndipo Yesu anadza nalankhula nao, nanena, Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi pa dziko lapansi.

Mateyu 28