Mateyu 26:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Ndipo ophunzira anacita monga Yesu anawauza, nakonza Paskha.

20. Ndipo pakufika madzulo, Iye analikukhala pacakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;

21. ndipo m'mene analinkudya, Iye anati, Indetu ndinena kwa inu, mmodzi wa inu adzandipereka Ine.

Mateyu 26