Mateyu 21:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yesu ananena kwa iwo, 1 Kodi simunawerenga konse m'malembo,Mwala umene anaukana omanga nyumbaWomwewu unakhala mutu wa pangondya:ici cinacokera kwa Ambuye,Ndipo ciri cozizwitsa m'maso mwathu?

Mateyu 21

Mateyu 21:38-46