3. Ndipo anaturuka dzuwa litakwera, naona ena ataima cabe pabwalo;
4. ndipo kwa iwo anati, Pitani inunso kumunda, ndipo ndidzakupatsani cimene ciri coyenera. Ndipo iwo anapita.
5. Ndiponso anaturuka usana, ndimonso popendeka dzuwa, nacita cimodzimodzi.