Mateyu 20:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Ndipo anaturuka dzuwa litakwera, naona ena ataima cabe pabwalo;

4. ndipo kwa iwo anati, Pitani inunso kumunda, ndipo ndidzakupatsani cimene ciri coyenera. Ndipo iwo anapita.

5. Ndiponso anaturuka usana, ndimonso popendeka dzuwa, nacita cimodzimodzi.

Mateyu 20