Mateyu 20:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pakuti Ufumu wa Kumwamba ufanana ndi munthu mwini banja, amene anaturuka mamawa kuka lembera anchito a m'munda wace wampesa.

2. Ndipo parnene adapangana ndi anchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza ku munda wace.

3. Ndipo anaturuka dzuwa litakwera, naona ena ataima cabe pabwalo;

Mateyu 20