Mateyu 19:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo panali pamene Yesu anatha mau amenewa, anacokera ku Galileya, nadza ku malire a Yudeya, a ku tsidya lija la Yordano.

2. Ndipo makamu akuru a anthu anamtsata; ndipo Iye anawaciritsa kumeneko.

3. Ndipo Afarisi anadza kwa Iye, namuyesa, nanena, Kodi nkuloledwa kuti munthu acotse mkazi wace pa cifukwa ciri conse?

Mateyu 19