Mateyu 14:26-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Koma m'mene ophunzirawo anamuona Iye, alikuyenda pamadzi, ananthunthumira, nati, ndi mzukwa! Ndipo anapfuula ndi mantha.

27. Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope.

28. Ndipo Petro anamyankha Iye nati, Ambuye, ngati ndinutu, mundiuze ndidze kwa lou pamadzi.

Mateyu 14