Mateyu 13:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Koma maso anu ali odala, cifukwa apenya; ndi makutu anu cifukwa amva.

17. Pakuti indetu ndinena kwa inu, kuti aneneri ambiri ndi anthu olungama analakalaka kupenya zimene muziona, koma sanaziona; ndi kumva zimene muzimva, koma sanazimva.

18. Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.

Mateyu 13