Mateyu 12:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Iye anati kwa iwo, Munthu ndani wa inu, amene ali nayo nkhosa imodzi, ndipo ngati idzagwa m'dzenje tsiku la Sabata, kodi sadzaigwira, ndi kuiturutsa?

Mateyu 12

Mateyu 12:9-15