44. Nasanduliza nyanja yao mwazi,Ndi mitsinje yao, kuti sangakhoze kumwa.
45. Anawatumizira pakati pao mitambo ya nchenche zakuwatha;Ndi acule akuwaononga.
46. Ndipo anapatsa mphuci dzinthu dzao,Ndi dzombe nchito yao.
47. Anapha mphesa zao ndi matalala,Ndi mikuyu yao ndi cisanu.