Masalmo 78:44-47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

44. Nasanduliza nyanja yao mwazi,Ndi mitsinje yao, kuti sangakhoze kumwa.

45. Anawatumizira pakati pao mitambo ya nchenche zakuwatha;Ndi acule akuwaononga.

46. Ndipo anapatsa mphuci dzinthu dzao,Ndi dzombe nchito yao.

47. Anapha mphesa zao ndi matalala,Ndi mikuyu yao ndi cisanu.

Masalmo 78