7. Onani abwetuka pakamwa pao;M'milomo mwao muli lupanga,Pakuti amati, Amva ndani?
8. Koma Inu, Yehova, mudzawaseka;Mudzalalatira amitundu onse.
9. Inu, mphamvu yanga, ndidzakulindirani;Pakuti Mulungu ndiye msanje wanga.
10. Mulungu wa cifundo canga adzandikumika:Adzandionetsa tsoka la adani anga.