Masalmo 46:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Cinkana madzi ace akokoma, nacita thobvu,Nagwedezeka mapiri ndi kudzala kwace.

4. Pali mtsinje, ngalande zace zidzakondweretsa mudzi wa Mulungu.Malo oyera okhalamo Wam'mwambamwamba,

5. Mulungu ali m'kati mwace, sudzasunthika:Mulungu adzauthandiza mbanda kuca.

Masalmo 46