Masalmo 34:15-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Maso a Yehova ali pa olungama mtima,Ndipo makutu ace achereza kulira kwao.

16. Nkhopeya Yehovaitsutsananao akucita zoipa,Kudula cikumbukilo cao pa dziko lapansi.

17. Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva,Nawalanditsa ku masautso ao onse.

18. Yehova ali pafupi ndi iwo a mtimawosweka,Apulumutsa iwo a mzimu wolapadi,

Masalmo 34