Masalmo 29:5-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Liu la Yehova lithyola mitengo yamkungudza;Inde Yehova athyola mikungudza ya ku Lebano.

6. Aitumphitsa monga mwana wa ng'ombe;Lebano ndi Sirio monga msona wa njati.

7. Liu la Yehova ligawa malawi a moto.

8. Liu la Yehova ligwedeza cipululu;Yehova agwedeza cipululu ca Kadese.

Masalmo 29