Masalmo 27:12-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Musandipereke ku cifuniro ca akundisautsa;Cifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zaciwawa.

13. Ndikadapanda kukhulupirira kuti ndikaone ubwino wa YehovaM'dziko la amoyo, ndikadatanil

14. Yembekeza Yehova:Limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako;Inde, yembekeza Yehova.

Masalmo 27