1. Munandisanthula, Yehova, nimundidziwa.
2. Inumudziwakukhalakwangandi kuuka kwanga,Muzindikira lingaliro langa muli kutali.
3. Muyesa popita ine ndi pogona ine,Ndi njira zanga zonse muzolowerana nazo.
4. Pakuti asanafike mau pa lilime langa,Taonani, Yehova, muwadziwa onse.