Masalmo 119:24-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. Mboni zanu zomwe ndizo zondikondwetsa,Ndizo zondipangira nzeru.

25. Moyo wanga umamatika ndi pfumbi;Mundipatse moyo monga mwa mau anu.

26. Ndinafotokozera njira zanga, ndipo munandiyankha:Mundiphunzitse malemba anu.

27. Mundizindikiritse njira ya malangizo anu;Kuti ndilingalire zodabwiza zanu.

28. Moyo wanga wasungunuka ndi cisoni:Mundilimbitse monga mwa mau anu.

Masalmo 119