132. Munditembenukire, ndi kundicitira cifundo,Monga mumatero nao akukonda dzina lanu.
133. Kfiazikitsanimapaziangam'mau anu;Ndipo zisandigonjetse zopanda pace ziri zonse.
134. Mundiombole ku nsautso ya munthu:Ndipo ndidzasamalira malangizo anu.
135. Muwalitse nkhope yanu pa mtumiki wanu;Ndipo mundiphunzitse malemba anu.